Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 62
  • Nyimbo Yatsopano

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nyimbo Yatsopano
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Imbani Chitamando cha Yehova Molimbika!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tidzakhala Ndi Moyo Wosatha
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 62

NYIMBO 62

Nyimbo Yatsopano

Losindikizidwa

(Salimo 98)

  1. 1. Imbira M’lungu, imba nyimbo yatsopano.

    Unene kwa onse ntchito zake zonse.

    Umutamande, Mulungu ndi wopambana.

    Ndi wachilungamo

    Poweruza anthu.

    (KOLASI)

    Imbani

    Nyimbo yatsopano.

    Imbani,

    Yehova ndi Mfumu.

  2. 2. Mosangalala fuula kwa Mfumu yathu.

    Muzimutamanda ndi nyimbo yokoma.

    Tiyeni tonse timuimbire mokweza.

    Zeze ndi lipenga

    Ziimbe pamodzi.

    (KOLASI)

    Imbani

    Nyimbo yatsopano.

    Imbani,

    Yehova ndi Mfumu.

  3. 3. Nyanja ndi zonse mmenemo zimutamande.

    Zolengedwa zake zizimutamanda.

    Dziko lapansi nalonso limutamande.

    Mapiri ndi zigwa

    Zimutamandenso.

    (KOLASI)

    Imbani

    Nyimbo yatsopano.

    Imbani,

    Yehova ndi Mfumu.

(Onaninso Sal. 96:1; 149:1; Yes. 42:10.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena