Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 149
  • Tiimbire Yehova Chifukwa Wapambana

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tiimbire Yehova Chifukwa Wapambana
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tiimbire Yehova Chifukwa Wapambana
    Imbirani Yehova
  • Ufumu wa Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova
  • Dzina la Atate Wathu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 149

NYIMBO 149

Tiimbire Yehova Chifukwa Wapambana

Losindikizidwa

(Ekisodo 15:1)

  1. 1. Timuimbire Yehova M’lungu wokwezeka.

    Waponya Aiguputo onyada m’nyanja.

    Mutamandeni

    Palibenso Mulungu wina.

    Yehova ndi dzina lake,

    Wapambanadi.

    (KOLASI)

    Yehova ndinu wokwezeka.

    Simunasinthe ndinudi Mfumu.

    Mudzagonjetsa adani onse

    N’kuyeretsa dzina lanu.

  2. 2. Mitundu yonse

    ikutsutsana ndi Yehova.

    Ichita manyazi Ngakhale

    ndi yamphamvu.

    Iwonongedwa Singathawe

    Aramagedo.

    Idzadziwa kuti Mulungu ndi Yehova.

    (KOLASI)

    Yehova ndinu wokwezeka.

    Simunasinthe ndinudi Mfumu.

    Mudzagonjetsa adani onse

    N’kuyeretsa dzina lanu.

(Onaninso Sal. 2:​2, 9; 92:8; Mal. 3:6; Chiv. 16:16.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena