Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 139
  • Yerekezerani Kuti Muli M’dziko Latsopano

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yerekezerani Kuti Muli M’dziko Latsopano
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Yerekezerani Kuti Muli M’dziko Latsopano
    Imbirani Yehova
  • Tiimbile Limodzi Nyimbo ya Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tiyeni Tiimbe Nyimbo ya Ufumu!
    Imbirani Yehova
  • M’patseni Yehova Ulemerero
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 139

NYIMBO 139

Yerekezerani Kuti Muli M’dziko Latsopano

Losindikizidwa

(Chivumbulutso 21:​1-5)

  1. 1. Yerekeza ukuona

    Tonse tili m’dziko latsopano.

    Ona mmene udzamvere

    Kukhala m’dziko lamtendere.

    Oipa onse adzatha.

    M’lungu wathu sadzalephera,

    Adzasinthadi zinthu padzikoli.

    Tidzamuimbira

    nyimbo tikumati:

    (KOLASI)

    “Tikuthokoza mwachita bwino.

    Zonse zakhaladi zatsopano.

    Tikuimba nyimbo mwachisangalalo

    Ndinudi woyenera ulemerero.”

  2. 2. Taganizira m’tsogolo

    Tonse tili m’dziko latsopano.

    Sitidzamva ndi kuona

    Zinthu zotichititsa mantha.

    Zomwe M’lungu walonjeza

    Zonse zidzakwaniritsidwa.

    Adzaukitsanso anthu akufa,

    Iwo ndi ife

    tidzamuyamikira.

    (KOLASI)

    “Tikuthokoza mwachita bwino.

    Zonse zakhaladi zatsopano.

    Tikuimba nyimbo mwachisangalalo

    Ndinudi woyenera ulemerero.”

(Onaninso Sal. 37:​10, 11; Yes. 65:17; Yoh. 5:​28; 2 Pet. 3:​13.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena