Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 94
  • Tikuthokoza Mulungu Potipatsa Mawu Ake

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tikuthokoza Mulungu Potipatsa Mawu Ake
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tikuyamikira Mulungu Kuti Anatipatsa Mawu Ake
    Imbirani Yehova
  • Khulupirirani Mawu a Yehova
    Nsanja ya Olonda—2005
  • “Muziyamika pa Chilichonse”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
  • Lolani Kuti Mawu a Mulungu Aunike Njira Yanu
    Nsanja ya Olonda—2005
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 94

NYIMBO 94

Tikuthokoza Mulungu Potipatsa Mawu Ake

Losindikizidwa

(Afilipi 2:16)

  1. 1. Yehova Atate tikuthokoza

    Chifukwa mwatipatsa mawu anu.

    Munawauziradi.

    Anatimasula.

    Kuwala kwake kwatipatsa nzeru.

  2. 2. Mawu anu onse ndi a mphamvudi.

    Amatithandiza kusankha bwino

    Ndiponso zigamulo

    Zanu n’zolondola.

    Mfundo zanu zimatitsogolera.

  3. 3. Mawu anu amatikhudza mtima.

    Aneneri ankakhulupirira,

    Nafe tithandizeni

    Tikhulupirire.

    Tikuthokoza mwatipatsa mawu.

(Onaninso Sal. 19:9; 119:​16, 162; 2 Tim. 3:16; Yak. 5:17; 2 Pet. 1:21.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena