Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 159
  • M’patseni Yehova Ulemerero

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • M’patseni Yehova Ulemerero
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tiimbile Limodzi Nyimbo ya Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tiyeni Tiimbe Nyimbo ya Ufumu!
    Imbirani Yehova
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 159

NYIMBO 159

M’patseni Yehova Ulemerero

Losindikizidwa

(Salimo 96:8)

  1. 1. Yehova, palibe munthu

    Angafanane nanu.

    N’dzakubwezerani chani

    Pa zonse mumandipatsa?

    Ndikayang’ana kumwamba,

    Ndimaonatu mphamvu.

    Ndine wotsika Yehova

    Koma m’mandiganizira.

    (KOLASI)

    Ndikuimba, ndimveni Yehova.

    Ndikukutamandani.

    M’lungu wanga, Mfumu yamuyaya.

    Ndinu woyeneradi

    Ulemerero wonse.

  2. 2. Zochita zanga Yehova

    Zikulemekezeni.

    Ndizilengeza uthenga

    Ndi ntchito zanu zabwino.

    Kukutumikiranitu

    Kumandisangalatsa.

    Muzindipatsabe mphamvu

    Muzinditsogolerabe.

    (KOLASI)

    Ndikuimba, ndimveni Yehova.

    Ndikukutamandani.

    M’lungu wanga, Mfumu yamuyaya.

    Ndinu woyeneradi

    Ulemerero wonse.

  3. 3. Nyanja, zitunda ndi zigwa,

    Dzuwa, mwezi, nyenyezi,

    Zimanditsimikizira

    Chikondi chanu chosatha.

    Ulemu ndi kukongola

    Ndi zomwe ndimaona.

    Sindingachitire mwina

    Koma kukulambirani.

    (KOLASI)

    Ndikuimba, ndimveni Yehova.

    Ndikukutamandani.

    M’lungu wanga, Mfumu yamuyaya.

    Ndinu woyeneradi

    Ulemerero wonse.

(Onaninso Sal. 96:1-10; 148:3, 7.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena