Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • bi12 tsamba 1952
  • 13 Miyezi ya Kalendala ya M’Baibulo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • 13 Miyezi ya Kalendala ya M’Baibulo
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
13 Miyezi ya Kalendala ya M’Baibulo

13 Miyezi ya Kalendala ya M’Baibulo

Mwezi wa Ayuda unali kuyambira pamene mwezi weniweni wakhala, kukafika pamene mwezi wotsatira wakhala.—Yes. 66:23.

MIYEZI

NYENGO

MBEWU

Yopatulika

Yanthawi zonse

   

1

7

Yorodano asefukira chifukwa cha mvula ndi chipale chofewa

Kukolola fulakesi. Kuyamba kukolola balere

2

8

Chilimwe chiyamba. Kawirikawiri kuthambo kumakhala kopanda mitambo

Kukolola balere. Kukolola tirigu m’madera otsika

3

9

Kunja kumatentha. Mpweya wabwino

Kukolola tirigu. Nkhuyu zoyambirira. Maapulo ena

4

10

Kutentha kumawonjezeka. Kumagwa mame ambiri

Mphesa zoyambirira. Zomera ndi akasupe zimauma

5

11

Kutentha kumafika pachimake

Kuyamba kukolola mphesa

6

12

Kutentha kumapitirizabe

Kukolola mphesa ndi nkhuyu za m’chilimwe

7

1

Chilimwe chikutha. Mvula yoyambirira imagwa

Kumaliza kukolola. Kuyamba kulima

8

2

Mvula yowaza

Kubzala tirigu ndi balere. Kukolola maolivi

9

3

Mvula imawonjezeka. Madzi amaundana. Chipale chofewa chimagwa m’mapiri

Udzu umakula

10

4

Kumazizira kwambiri. Kumagwa mvula. Chipale chofewa chimagwa m’mapiri

Zigwa zimakhala zobiriwira. Mbewu zimachita maluwa

11

5

Kuzizira kumachepa. Mvula imapitiriza kugwa

Amondi amachita maluwa. Mitengo ya mkuyu imaphukira

12

6

Kumachita mabingu ndi mvula yamatalala

Karobu amachita maluwa. Kukolola zipatso za m’gulu la malalanje

13

 

M’zaka 19 zilizonse anali kuwonjezera mwezi wina wapadera maulendo 7. Kawirikawiri umenewu unali mwezi wachiwiri wa Adara (Veadara)

(Onani m’Baibulo lenileni kuti mumvetse izi)

1 NISANI (ABIBU) March—April

14 Pasika

15-21 Mkate Wopanda Chofufumitsa

16 Nsembe ya zipatso zoyamba kucha

Balere

2 IYARA (ZIVI) April—May

Pa 14 Pasika Wochitika Nthawi Yake Itadutsa (Nu 9:10-13)

Tirigu

3 SIVANI May—June

Pa 6 Chikondwerero cha Masabata (Pentekosite)

Nkhuyu Zoyambirira

4 TAMUZI June—July

Mphesa Zoyambirira

5 ABA July—August

Zipatso za M’chilimwe

6 ELULI August—September

Mphesa, Nkhuyu

7 TISHIRI (ETANIMU) September—October

Pa 1 Tsiku loliza lipenga

Pa 10 Mwambo Wophimba Machimo

Pa 15-21 Chikondwerero cha Misasa kapena kuti Chikondwerero cha Zokolola

Pa 22 Msonkhano wapadera

Kulima

8 HESHIVANI (BULU) October—November

Maolivi

9 KISILEVI November—December

Pa 25 Chikondwerero cha Kupereka Kachisi kwa Mulungu

Ziweto zili m’khola nyengo yachisanu

10 TEBETI December—January

Zomera Zikukula

11 SEBATI January—February

Amondi Wachita Maluwa

12 ADARA February—March

Pa 14, 15 Purimu

Malalanje

13 VEADARA March

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena