Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g05 4/8 tsamba 32
  • Mayankho Othandiza a Mafunso Amene Mwakhala Mukufunsa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mayankho Othandiza a Mafunso Amene Mwakhala Mukufunsa
  • Galamukani!—2005
Galamukani!—2005
g05 4/8 tsamba 32

Mayankho Othandiza a Mafunso Amene Mwakhala Mukufunsa

• Kodi n’chifukwa ninji makolo anga samandimvetsetsa?

• Kodi n’chifukwa ninji amayi ndi atate analekana?

• Kodi ndingapange motani mabwenzi enieni?

• Kodi n’chifukwa ninji ndimachita tondovi kwambiri?

• Kodi n’chifukwa ninji achichepere samaleka kundivutitsa?

• Bwanji ponena za kugonana ukwati usanachitike?

Buku lakuti Mafunso Achichepere Akufunsa—Mayankho Amene Amathandiza n’losiyana ndi mabuku ena a achinyamata. Nkhani zimene anazilemba m’buku limeneli anazisankha atakambirana ndi achinyamata ambirimbiri padziko lonse lapansi. Ndipo mayankho ake ochokera m’Baibulo, lomwe ndi Mawu a Mulungu, amathandizadi. Mafunso ali pamwambawa ndi ena chabe mwa mafunso amene buku la masamba 320 limeneli limayankha.

Ngati mukufuna kuitanitsa bukuli, lembani zofunika m’mizere ili m’munsiyi ndipo tumizani ku adiresi imene ili pomwepoyo kapena ku adiresi yoyenera imene ili patsamba 5 la magazini ino.

□ Popanda kulonjeza kuti ndidzachita chilichonse, ndikupempha kuti munditumizire buku la Mafunso Achichepere Akufunsa—Mayankho Amene Amathandiza.

□ Chonde nditumizireni munthu kuti ayambe kuchita nane phunziro la Baibulo lapanyumba laulere.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena