Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 3/07 tsamba 32
  • Mwambo Wosafunika Kuuphonya

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mwambo Wosafunika Kuuphonya
  • Galamukani!—2007
Galamukani!—2007
g 3/07 tsamba 32

Mwambo Wosafunika Kuuphonya

“Muzichita zimenezi pondikumbukira ine.” Mawu amenewa a Ambuye wathu Yesu Khristu, opezeka pa Luka 22:19, ananenedwa pa nthawi imene Yesu anakhazikitsa mwambo wa Chikumbutso cha imfa yake. Imfa ya Yesu ndi imene inatsegula njira yakuti anthu akhale ndi chiyembekezo chodzakhala ndi moyo wosatha m’Paradaiso. Choncho m’poyenera kuti tizikumbukira imfa yake.

Kodi mudzapezeka pa Chikumbutso cha chaka chino?

Dzapiteni ku mwambo wofunikawu womwe a Mboni za Yehova akukuitanirani. Mwambowu udzayamba dzuwa litalowa pa tsiku la Nisani 14, mu kalendala ya Baibulo. Chaka chino tsikuli ndi Lolemba, pa April 2. Mboni za Yehova za kwanuko zingakuuzeni malo ndi nthawi yeniyeni imene mwambowu udzakhaleko m’dera lanu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena