Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 10/08 tsamba 3
  • Kodi Mwana Wanu Amagwiritsa Ntchito Intaneti?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mwana Wanu Amagwiritsa Ntchito Intaneti?
  • Galamukani!—2008
  • Nkhani Yofanana
  • Ana Akamagwiritsa Ntchito Intaneti Zimene Makolo Angachite
    Galamukani!—2008
  • Kuthandiza Achinyamata Kukhalabe Okhulupirika
    Galamukani!—2007
  • Kodi Ndi Bwino Kucheza pa Intaneti?
    Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Lachiwiri
  • Ana Akamagwiritsa Ntchito Intaneti Zimene Makolo Ayenera Kudziwa
    Galamukani!—2008
Onani Zambiri
Galamukani!—2008
g 10/08 tsamba 3

Kodi Mwana Wanu Amagwiritsa Ntchito Intaneti?

PANTHAWI iliyonse ndiponso kulikonse, kaya kunyumba, kusukulu, kwa anzawo, pafoni ya m’manja ndi pa zipangizo zina, ana ambirimbiri amagwiritsa ntchito Intaneti. Ngati ndinu kholo, mwinanso mwana wanu akuchita zimenezi, ndipo n’kutheka kuti amadziwa zambiri kuposa inuyo. Mwinanso amadziwa kubisa zimene iye amachita pa Intaneti.

Zimenezi n’zodetsa nkhawa, koma sikuti palibe chimene tingachite ndi vutoli. N’zoona, zingaoneke kuti mwana wanu amaidziwa bwino Intaneti kuposa inuyo. Komabe inunso mungathe kudziwa zina ndi zina zokhudza Intaneti. Ndipo sikuti mukufunikira kukhala katswiri wa chilichonse chokhudza Intaneti kuti muteteze mwana wanu.

Nkhaniyi ili ndi mfundo zimene zingakuthandizeni. Choyamba, tiyeni tione ena mwa mavuto amene mwana wanu angakumane nawo pa Intaneti.

[Mawu Otsindika patsamba 3]

Ku Canada pafupifupi theka la achinyamata amene ali ndi foni za m’manja, amagwiritsa ntchito Intaneti pafonizo

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena