Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 8/10 tsamba 32
  • Kodi Mboni za Yehova Zimaphunzitsa Bwanji Baibulo?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mboni za Yehova Zimaphunzitsa Bwanji Baibulo?
  • Galamukani!—2010
Galamukani!—2010
g 8/10 tsamba 32

Kodi Mboni za Yehova Zimaphunzitsa Bwanji Baibulo?

Zimakambirana ndi anthu nkhani zosiyanasiyana za m’Baibulo ndipo nthawi zambiri zimagwiritsa ntchito buku lakuti Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni? M’bukuli muli mitu 19 ndipo ina mwa mituyi ndi yakuti:

“Kodi Zoona Zenizeni za Mulungu N’zotani?”

“Kodi Yesu Kristu Ndani?”

“Kodi Akufa Ali Kuti?”

“Kodi Tili ‘M’masiku Otsiriza’?”

“N’chifukwa Chiyani Mulungu Amalola Kuti Anthu Azivutika?”

“Zimene Mungachite Kuti Banja Lanu Likhale ndi Moyo Wosangalala”

Ophunzira amaloledwa kufunsa mafunso ndipo amaona okha mayankho ake kuchokera m’Baibulo. Kenako mogwirizana ndi zimene aphunzira m’Baibulo, amasankha okha chipembedzo chimene akufuna.

Mukhoza kupempha kuti munthu aziphunzira nanu Baibulo. Mukhozanso kuitanitsa bukuli polemba adiresi yanu m’mizere ili m’munsiyi, ndipo tumizani ku adiresi yomwe ili pomwepoyo kapena tumizani ku adiresi yoyenera yomwe ili patsamba 5 m’magazini ino.

□ Ndikupempha kuti munditumizire bukuli.

□ Nditumizireni munthu kuti ayambe kuphunzira nane Baibulo kwaulere.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena