Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 4/12 tsamba 32
  • Kodi Mungatani Kuti Mudziwe Mulungu Woona?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mungatani Kuti Mudziwe Mulungu Woona?
  • Galamukani!—2012
Galamukani!—2012
g 4/12 tsamba 32

Kodi Mungatani Kuti Mudziwe Mulungu Woona?

● Kuyambira kale kwambiri anthu akhala akufunafuna Mulungu woona. Zimenezi zachititsa kuti akhale ndi maganizo osiyanasiyana okhudza Mulungu. N’chifukwa chake masiku ano pali zipembedzo zambiri. Komano kodi mungatani kuti mudziwe Mulungu woona?

Buku lakuti Mankind’s Search for God lingakuthandizeni. Munthu wina wa ku Mexico, yemwe amalemba mabuku, anati: “Ngakhale kuti bukuli ndi laling’ono moti munthu akhoza kungoliika m’thumba, lili ndi mfundo zothandiza kwambiri. Bukuli litaikidwa mu laibulale pamodzi ndi mabuku ena osiyanasiyana okwana 90,000, munthu akhoza kusankha kuwerenga buku limeneli.”

Mukhoza kuitanitsa buku la masamba 384 limeneli polemba zofunika m’mizere ili m’munsiyi ndi kutumiza ku adiresi yoyenera pa ma adiresi amene ali patsamba 5 m’magazini ino.

□ Ndikupempha kuti munditumizire bukuli.

□ Nditumizireni munthu kuti ayambe kuphunzira nane Baibulo kwaulere.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena