Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • yp2 tsamba 244-245
  • Zosangalatsa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zosangalatsa
  • Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Lachiwiri
  • Nkhani Yofanana
  • Mfundo Zanga—Zosangalatsa
    Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Lachiwiri
  • Kodi Zimene Mumachita pa Nthawi Yosangalala Zimakhala Zopindulitsa?
    Nsanja ya Olonda—2011
  • Zosangalatsa Zomwe Zimatsitsimula
    Nsanja ya Olonda—2006
  • Musalole Chilichonse Kusokoneza Ubwenzi Wanu ndi Yehova
    Nsanja ya Olonda—2013
Onani Zambiri
Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Lachiwiri
yp2 tsamba 244-245

Chigawo 8

Zosangalatsa

Kodi mumachita kangati zinthu zosangalatsa, monga kuchita masewera olimbitsa thupi, kumvera nyimbo, kuonera TV ndi kuchita masewera a pakompyuta?

□ Mwa apo ndi apo

□ Kamodzi patsiku

□ Kangapo patsiku

Kodi ndani amakuchititsani kusankha zosangalatsa zimene mumakonda?

□ Anzanu

□ Makolo anu

□ Oitanira malonda

Masiku ano kuli zosangalatsa zambiri zimene achinyamatanu mungasangalale nazo. Koma nthawi imene muli nayo ndi yochepa. Ndipo zosangalatsa zimene mungasankhe zingakhudze khalidwe lanu komanso mmene mumaganizira. Choncho, kodi mungasankhe bwanji zosangalatsa zoyenera? Ndipo kodi muyenera kuzichita nthawi yochuluka bwanji? Mitu 30 mpaka 33 ikuthandizani kudziwa mmene mungasankhire zosangalatsa zabwino.

[Chithunzi chachikulu pamasamba 244, 245]

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena