Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 118
  • Landiranani

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Landiranani
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Tizilandilana
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • ‘Landiranani’!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Achititseni Kudzimva Olandiridwa pa Chikumbutso
    Utumiki Wathu wa Ufumu—1994
  • Kulandira Mfumu Yakudzayo!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 118

Nyimbo 118

Landiranani

Losindikizidwa

(Aroma 15:7)

1. Takulandirani inu nonse.

Mwasonkhana kuti m’phunzire.

Cho’nadi M’lungu amatipatsa

Timavomera akamatiitana.

2. Tikuyamikira abalewa

Chifukwa amatilandira.

Ndi amenewa tizikondana,

Tilandirenso ena odzasonkhana.

3. Aliyense akuitanidwa

Ndi M’lungu kudzaphunzitsidwa.

M’lungu watikokera kwa Iye

Choncho landiranani ndi mtima wonse.

(Onaninso Yoh. 6:44; Afil. 2:29; Chiv. 22:17.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena