Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 67
  • Muzipemphera kwa Yehova Tsiku Lililonse

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzipemphera kwa Yehova Tsiku Lililonse
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Muzipemphera kwa Yehova Nthawi Zonse
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Pempherani kwa Yehova Tsiku ndi Tsiku
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kuyandikira kwa Mulungu m’Pemphero
    Kodi Mulungu Amafunanji kwa Ife?
  • Yesu Atiphunzitsa Ife Kupemphera
    Kumamumvetsera Mphunzitsi Wamkuru’yo
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 67

Nyimbo 67

Muzipemphera kwa Yehova Tsiku Lililonse

Losindikizidwa

(1 Atesalonika 5:17)

1. Pemphera kwa Yehova amamva.

Ndi mwayi umene watipatsa.

Mu’ze zakukhosi monga mnzako,

Ndi wodalirika, bwenzi lako.

Pempherabe kwa M’lungu.

2. Pemphera kwa M’lungu uthokoze.

Um’pemphe akukhululukire.

Timuuze zakukhosi kwathu,

Amadziwa zofooka zathu.

Pempherabe kwa M’lungu.

3. Pemphera kwa M’lungu zikavuta,

Ndi Tate wathu akuthandiza.

Um’pemphe kuti akuteteze,

Um’khulupirire usaope.

Pempherabe kwa M’lungu.

(Onaninso Mat. 6:9-13; 26:41; Luka 18:1.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena