Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 72
  • Tizisonyeza Chikondi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tizisonyeza Chikondi
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Tikulitse Khalidwe la Chikondi
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kulani M’chikondi
    Nsanja ya Olonda—2001
  • Chikondi Ndi Khalidwe Lamtengo Wapatali Kwambiri
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Khalani Ndi Chikondi Chimene Sichitha Konse
    Nsanja ya Olonda—2009
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 72

Nyimbo 72

Tizisonyeza Chikondi

Losindikizidwa

(1 Akorinto 13:1-8)

1. Tikupemphera kwa Mulungu,

Kuti tizikonda anzathu.

Tikakhala ndi mzimu wake

Ndiye kuti tingakondane.

Tingakhale ndi luso, nzeru,

Komabe osakonda anthu.

Izi sizingatithandize.

Choncho chikondi tikulitse.

2. Tisadalire nzeru zokha

Pamene tiphunzitsa nkhosa.

Ndi kofunika kuzikonda

Kuti cho’nadi chizilowa.

Ngakhale tikalakwiridwa

Tidzakhalabe opirira.

Chikondi chipirira zonse

Ndiponso sichidzatha konse.

(Onaninso Yoh. 21:17; 1 Akor. 13:13; Agal. 6:2.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena