Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 78
  • Kuleza Mtima

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kuleza Mtima
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • “Khalani Oleza Mtima”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • ‘Valani Kuleza Mtima’
    Nsanja ya Olonda—2001
  • Yehova Ndi Mulungu Woleza Mtima
    Nsanja ya Olonda—2001
  • Khalani Oleza Mtima pa Onse
    Nsanja ya Olonda—1991
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 78

Nyimbo 78

Kuleza Mtima

Losindikizidwa

(Agalatiya 5:22)

1. Yehova Mbuye wathu

Amakonda dzina lake.

Amafunitsitsadi

Kuti lisamanyozedwe.

Kwanthawi yaitali

Wakhala ’kupirira.

Iyetu sanatope

Amaleza mtima.

Anthu m’mitundu yonse

Amafuna ’pulumuke.

Kuleza kwake mtima

Sikudzapita pachabe.

2. Kuti tisapatuke

Tikhale oleza mtima.

Tidzapeza mtendere

N’kupewa kumangokwiya.

Pochita ndi anzathu

Tidzaona zabwino,

N’kukhala odziletsa

Ngakhale m’mavuto.

Kuleza mtima kwathu

Ndiko kudzatithandiza

Kutsanzira Mulungu

Amene tikumudziwa.

(Onaninso Eks. 34:14; Yes. 40:28; 1 Akor. 13:4, 7; 1 Tim. 2:4.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena