Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • rr tsamba 56-57
  • “Iwe Mwana wa Munthu, Kodi Waona Zimenezi?”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Iwe Mwana wa Munthu, Kodi Waona Zimenezi?”
  • Yehova Wabwezeretsa Kulambira Koyera
  • Nkhani Yofanana
  • “Uone Zinthu Zoipa Ndi Zonyansa Zimene Anthu Akuchita”
    Yehova Wabwezeretsa Kulambira Koyera
  • Peŵani Kulambira Mafano Kwamtundu Uliwonse
    Nsanja ya Olonda—1993
  • Kufukiza Kodi N’kofunika pa Kulambira Koona?
    Nsanja ya Olonda—2003
  • Yerusalemu Aonongedwa
    Bukhu Langa la Nkhani za Baibulo
Onani Zambiri
Yehova Wabwezeretsa Kulambira Koyera
rr tsamba 56-57

BOKOSI 5A

“Iwe Mwana Wa Munthu, Kodi Waona Zimenezi?”

Losindikizidwa

Zinthu 4 zonyansa kwambiri zimene Ezekieli anaona m’bwalo la mkati la kachisi. (Ezek. 8:5-16)

Ayuda opanduka agwada n’kumalambira fano.

1. FANO LOIMIRA NSANJE

Ezekieli akuyang’ana m’bwalo lamkati la kachisi kumene akuluakulu a Yuda akupereka nsembe zofukiza kwa chifaniziro cha mulungu wabodza chimene anachigoba pakhoma.

2. AKULUAKULU 70 AKUPEREKA NSEMBE ZOFUKIZA KWA MILUNGU YABODZA

Azimayi akulirira mulungu wotchedwa Tamuzi.

3. ‘AZIMAYI AKULIRIRA MULUNGU WOTCHEDWA TAMUZI’

Amuna 25 ali m’bwalo lam’kati la kachisi ndipo akulambira dzuwa.

4. AMUNA 25 ‘AKUGWADIRA DZUWA’

Bwererani ku mutu 5, onani ndime 7-18

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena