Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w12 2/1 tsamba 16-17
  • Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
  • Nsanja ya Olonda—2012
  • Nkhani Yofanana
  • Phunziro 1
    Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
  • Mapiko a Gulugufe
    Galamukani!—2014
  • Mapiko a Gulugufe
    Galamukani!—2012
  • Luso la Gulugufe Woyera Lotha Kuimitsa Mapiko Ake Ngati V
    Kodi Zinangochitika Zokha?
Onani Zambiri
Nsanja ya Olonda—2012
w12 2/1 tsamba 16-17

Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo

ANA AZAKA ZOSAPITIRIRA ZITATU

Kodi ndani analenga dziko lapansili?

Kodi ndani analenga nyanja?

Kodi ndani analenga iwe ndi ine?

Kodi ndani analenga gulugufe yemwe ndi wokongola kwambiri?

Yehova Mulungu ndi amene analenga zinthu zonse Chivumbulutso 4:11

ZOTI MAKOLO ACHITE

Phunzitsani mwana wanu zinthu izi:

Kodi dzina la Mulungu ndani?

Kodi Yehova amakhala kuti?

Kodi Yehova analenga zinthu ziti?

Muuzeni mwana wanuyo kuti aloze:

Nyenyezi

Mitambo

Dzuwa

Boti

Dziko

Nyumba

Nyanja

Gulugufe

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena