Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w13 12/15 tsamba 32
  • Mlozera Nkhani wa Nsanja ya Olonda 2013

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mlozera Nkhani wa Nsanja ya Olonda 2013
  • Nsanja ya Olonda—2013
Nsanja ya Olonda—2013
w13 12/15 tsamba 32

Mlozera Nkhani wa Magazini a Nsanja ya Olonda a 2013

Wosonyeza deti la magazini imene muli nkhaniyo

BAIBULO

  • Chuma Chobisika kwa Zaka Zambiri (Baibulo la Chijojiya), 6/11

  • Kodi Lili ndi Uthenga Wotani? 10/11

  • N’zotheka Kulimvetsa, 4/1

BAIBULO LIMASINTHA ANTHU

  • ‘Ankafuna Kuti Ndione Ndekha Zoona’ (L. Alifonso), 2/1

  • ‘Anthu Ankadana Nane’ (W. Moya), 10/1

  • ‘Ndilibenso Maganizo Ofuna Kusintha Zinthu’ (J. Sylgren), 7/1

  • ‘Ndinali Wachiwawa’ (E. Leinonen), 4/1

  • “Ndinapeza Ufulu Weniweni” (B. Hewitt), 1/1

  • ‘Ndinayamba Kuganizira za Moyo Wanga’ (A. Hancock), 8/1

  • “Ndinkafuna Kudzakhala Wansembe” (R. Pacheco), 5/1

MAFUNSO OCHOKERA KWA OWERENGA

  • ‘Analalikira kwa Mizimu Imene Inali M’ndende’ (1Pet. 3:19), 6/15

  • Kodi Aisiraeli ankapha oipa powapachika pamtengo? 5/15

  • Kodi “ana a Mulungu woona” anali ndani? (Gen. 6:2, 4), 6/15

  • Kodi makolo azikhala ndi mwana wochotsedwa pa misonkhano? 8/15

  • N’chifukwa chiyani Yesu anagwetsa misozi? (Yoh. 11:35), 9/15

MBIRI YA MOYO WANGA

  • Ndife Osauka Koma Olemera (A. Ursu), 9/1

  • Ndinadalitsidwa Chifukwa Chomvera Yehova (E. Piccioli), 6/15

  • Ndinasankha Kutumikira Yehova (B. Walden), 12/1

  • “Ndinkaona, Koma Sindinkadziwa Tanthauzo” (O. Hamel), 3/1

  • Tachita Utumiki wa Nthawi Zonse kwa Zaka 50 Kumpoto (A. and A. Mattila), 4/15

  • Tadalitsidwa Chifukwa Chodalira Yehova (M. Allen), 10/15

  • Timasangalala Kutumikira Yehova Kulikonse (M. and J. Hartlief), 7/15

  • Yehova ‘Amanyamula Katundu Wanga’ (M. du Raan), 8/15

  • Zimene Zatithandiza Kukhalabe Osangalala (P. Smith), 5/15

MBONI ZA YEHOVA

  • Anabala Zipatso Chifukwa Chokonzekera Bwino (Chile), 1/15

  • Anadzipereka ku Mexico, 4/15

  • Anadzipereka ku Norway, 1/15

  • Anadzipereka ku Philippines, 10/15

  • Kutumikira Mulungu Kuli Ngati Mankhwala Ake, 11/15

  • Kwa Owerenga Magazini Athu (Nsanja ya Olonda), 1/1

  • M’bale Watsopano M’Bungwe Lolamulira (M. Sanderson), 7/15

  • Mfumu Inasangalala Kwambiri (Swaziland), 8/15

  • Msonkhano Wachigawo Wakuti ‘Mawu a Mulungu Ndi Choonadi’, 5/1

  • Musataye Mtima, 3/15

  • “Ngati Kamba Woyenda ndi Chigoba Chake” (makalavani), 11/15

  • Okhulupirika pa “Ola la Kuyesedwa” (Nkhondo yoyamba), 5/15

  • ‘Sewero la Chilengedwe la pa Nthawi Yake,’ 2/15

  • Yehova Anawateteza Pamene Ankazemba (Nazi), 12/15

  • “Zithunzi Zokongola Kwambiri,” 7/15

MOYO NDI MAKHALIDWE ACHIKHRISTU

  • Akulu—Kodi Mumalimbikitsa Anthu ‘Olefuka’? 6/15

  • Banja la Ana Opeza, 5/1

  • Kuti Musamakangane ndi Mwana Wanu, 11/1

  • Mabanja Akhoza Kukhala Osangalala Komanso Olimba, 9/1

  • Makolo—Phunzitsani Ana Anu Kuyambira Ali Akhanda, 8/15

  • Muchenjeze Anthu Ambiri, 10/15

  • Mwamuna Kapena Mkazi Wanu Akamwalira, 12/15

  • Mwana Wolumala, 2/1

  • Ngati Banja Latha, 10/1

  • Ngati Mwakwatiranso Kapena Kukwatiwanso, 7/1

  • Petulo ndi Hananiya Ananama—Tikuphunzirapo Chiyani? 3/1

  • Samalani ndi Zolinga za Mtima Wanu, 2/15

  • Tingaphunzire Chiyani kwa Munthu Wachifwamba? 6/1

  • Tizitonthozana, 3/15

NKHANI ZOPHUNZIRA

  • Abusa Tsanzirani Abusa Aakulu, 11/15

  • Akulu Achikhristu Ndi Antchito Anzathu Otipatsa Chimwemwe,’ 1/15

  • Anthu Okonda Yehova ‘Alibe Chowakhumudwitsa,’ 3/15

  • Chilengedwe Chimatithandiza Kukhulupirira Kwambiri Mulungu, 10/15

  • Cholowa Chathu Chochokera kwa Mulungu, 2/15

  • “Dziwani Kuti Ine Ndili Pamodzi ndi Inu Masiku Onse,” 7/15

  • Ganizirani za Mtundu wa Munthu Amene Muyenera Kukhala, 8/15

  • “Khalani Maso Kuti Musanyalanyaze Kupemphera,” 11/15

  • Khalanibe Otetezeka M’chigwa cha Yehova, 2/15

  • Kodi Abusa 7 ndi Atsogoleri 8 Akuimira Ndani Masiku Ano, 11/15

  • Kodi Muli ndi “Mtima Wodziwa” Yehova? 3/15

  • Kodi Mungapereke Chiyani pa Ntchito ya Ufumu? 12/15

  • Kodi Mwasandulika? 9/15

  • Kodi Ndinu “Odzipereka pa Ntchito Zabwino”? 5/15

  • Kodi Tikuphunzira Chiyani pa Pemphero Limene Linakonzedwa Bwino? 10/15

  • Kodi Timayamikira Cholowa Chathu Chochokera kwa Mulungu? 2/15

  • Kodi Zikumbutso za Yehova Zimakondweretsa Mtima Wanu? 9/15

  • Lolani Kuti Yehova Azikuumbani ndi Malangizo Ake, 6/15

  • Makhalidwe a Yehova Ndi Amtengo Wapatali, 6/15

  • Makolo ndi Ana Ayenera Kulankhulana Mwachikondi, 5/15

  • Mawu a Mulungu Azikuthandizani Ndipo Muzithandiza Nawo Ena, 4/15

  • “Musafulumire Kugwedezeka pa Maganizo Anu,” 12/15

  • “Musakwiyire Yehova,” 8/15

  • Musalole Chilichonse Kukulepheretsani Kupeza Ulemerero, 2/15

  • Musalole Chilichonse Kusokoneza Ubwenzi Wanu ndi Yehova, 1/15

  • “Musatope Kuchita Zabwino,” 4/15

  • “Muzichita Zimenezi Pondikumbukira,” 12/15

  • Muzichita Zinthu Mogwirizana ndi Pemphero la Yesu, 10/15

  • Muzigwira Bwino Ntchito Yanu Yolalikira, 5/15

  • Muzilankhulana Bwino Kuti Banja Lanu Likhale Lolimba, 5/15

  • Muzilemekeza Dzina Lalikulu la Yehova, 3/15

  • Muzimvera Abusa Amene Yehova Watipatsa, 11/15

  • Muzisankha Zinthu Mwanzeru Kuti Musataye Madalitso Anu, 5/15

  • Muzisankha Zochita Mwanzeru, 9/15

  • “Muzitsimikizira Kuti Zinthu Zofunika Kwambiri Ndi Ziti,” 4/15

  • Mwapatulidwa, 8/15

  • “Ndani Kwenikweni Amene Ali Kapolo Wokhulupirika ndi Wanzeru?” 7/15

  • Pitirizani Kuyandikira Yehova, 1/15

  • Pitirizani ‘Kuyembekezera Moleza Mtima’? 11/15

  • Popeza “Mwadziwa Mulungu” Kodi Muyenera Kuchita Chiyani? 3/15

  • “Tiuzeni, Kodi Zinthu Zimenezi Zidzachitika Liti?” 7/15

  • Tiziganizirana Ndiponso Kulimbikitsana, 8/15

  • ‘Tsikuli Lidzakhala Chikumbutso Chanu,’ 12/15

  • “Tumikirani Yehova Monga Akapolo,” 10/15

  • Tumikirani Yehova Popanda Kunong’oneza Bondo, 1/15

  • Ukhale Wolimba Mtima Chifukwa Yehova Ali Nawe, 1/15

  • Upainiya Umalimbitsa Ubwenzi Wanu ndi Mulungu, 9/15

  • Yehova Ndi Malo Anthu Okhalamo, 3/15

  • Yehova Ndi Wokhulupirika Ndiponso Amakhululuka, 6/15

  • Yehova Ndi Wowolowa Manja Ndiponso Wololera, 6/15

  • Yesu Anadyetsa Anthu Ambiri Kudzera mwa Anthu Ochepa, 7/15

  • Zikumbutso za Yehova Ndi Zodalirika, 9/15

  • Zimene Mungachite Kuti Muzipindula Powerenga Baibulo, 4/15

NKHANI ZOSIYANASIYANA

  • Anali Wochokera M’banja la Kayafa, 2/151

  • ‘Anaonedwa Ngati Wolungama’ (Rahabi), 11/11

  • Anapulumutsidwa “Pamodzi ndi Anthu Ena 7” (Nowa), 8/11

  • “Anayenda ndi Mulungu” (Nowa), 4/11

  • Anthu Ena Sanatchulidwe Mayina, 8/11

  • Ayuda Ankamanga Kampanda Padenga, 4/1

  • Elisa Anaona Magaleta Oyaka Moto, 8/15

  • “Iye Akulankhulabe” (Abele), 1/11

  • Kodi Josephus Analembadi Zimenezi? 3/15

  • Kodi Kachisi Anamangidwanso Pambuyo pa 70 C.E.? 4/151

  • Kodi Kaonekedwe ka Zinthu Kamakukhudzani Bwanji? 10/11

  • Kodi Kuonera Zolaula Kuli ndi Mavuto? 8/11

  • Kodi Mdyerekezi Anachokera Kuti? 2/11

  • Kodi Mulungu Angatikhululukire? 5/11

  • Kodi Ndani Amapita Kumwamba? 11/11

  • Kodi N’zoyenera Kupemphera kwa Oyera Mtima? 6/11

  • Kodi Tingathandize Bwanji Ena? 11/151

  • Kodi Zinenero Zinayambira pa “Nsanja ya Babele”? 9/11

  • Kodi Zipembedzo Mungazikhulupirire? 7/11

  • Kusiyanitsa Zinthu N’kothandiza, 9/151

  • Kutha kwa Dziko, 1/11

  • Kuukitsidwa, 10/11

  • Maliro a Ayuda M’nthawi ya Atumwi, 3/11

  • Mose, 2/11

  • Moyo Waphindu, 4/11

  • Moyo Wosatha, 7/11

  • Mtendere Padzikoli, 6/11

  • Mudzakumbamo Mkuwa, 12/11

  • N’chifukwa Chiyani Anthu Akuvutika Chonchi? 9/11

  • Nineve Unali “Mzinda Wokhetsa Magazi,” 4/11

  • Paulo Analalikira Msilikali Woteteza Mfumu, 2/151

  • Tsankho Likuchitika Padziko Lonse, 6/11

  • Uthenga Wabwino wa Yudasi, 2/11

YEHOVA

  • “Alibe Tsankho,” 6/11

  • ‘Amadzaza Mitima Yathu,’ 7/11

  • ‘Amakonda Wopereka Mokondwera,’ 9/11

  • ‘Amapereka Mphoto kwa Omufunafuna ndi Mtima Wonse,’ 11/11

  • Dzina, 1/11

  • Kodi Amakuganizirani? 5/1

  • Kodi Amamva Chisoni Tikamavutika? 7/1

  • Kodi Amamva Mapemphero Onse? 8/1

  • “Kodi Lamulo Loyamba ndi Liti?” 3/1

  • Kodi Ndi Wankhanza? 5/1

  • Kodi Timafunikiradi Mulungu? 12/1

  • Mabodza Omwe Amalepheretsa Anthu Kumukonda, 11/1

  • ‘Makhalidwe Ake Osaoneka Akuonekera,’ 8/1

  • “Mulungu wa Anthu Amoyo,” 2/1

  • “Mwaziulula kwa Tiana,” 1/1

  • “Pemphanibe,” 4/1

  • Tikhoza Kumukhumudwitsa, 9/1

  • “Yehova Anakukhululukirani,” 10/1

  • “Zonse Zimene Ndikupanga N’zatsopano,” 12/1

YESU KHRISTU

  • Kodi Analengedwa Liti? 3/1

  • Kodi Analonjeza Wochita Zoipa Kuti Akakhala Naye Kumwamba? 3/1

  • Kodi Tizimukumbukira Bwanji? 12/1

  • Kubweranso, 12/1

  • Kuika Maliro, 3/1

  • Kuukitsidwa, 3/1

  • N’chifukwa Chiyani Amatchedwa Mwana wa Mulungu? 3/1

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena