Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 October tsamba 1
  • Zimene Tinganene

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Tinganene
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • ●○○ ULENDO WOYAMBA
  • ○●○ ULENDO WOBWEREZA WOYAMBA
  • ○○● ULENDO WOBWEREZA WACHIWIRI
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Zimene Tinganene
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 October tsamba 1
A Mboni za Yehova akupatsana moni pa Nyumba ya Ufumu ku Malawi

Abale ndi alongo a ku Malawi akucheza pa Nyumba ya Ufumu

Zimene Tinganene

●○○ ULENDO WOYAMBA

Funso: Kodi timadziwa bwanji kuti mavuto amene timakumana nawo si chilango chochokera kwa Mulungu?

Lemba: Yak. 1:13

Funso la Ulendo Wotsatira: N’chifukwa chiyani timavutika?

○●○ ULENDO WOBWEREZA WOYAMBA

Funso: N’chifukwa chiyani timavutika?

Lemba: 1 Yoh. 5:19

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi Mulungu amamva bwanji akamationa tikuvutika?

○○● ULENDO WOBWEREZA WACHIWIRI

Funso: Kodi Mulungu amamva bwanji akamationa tikuvutika?

Lemba: Yes. 63:9

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi Mulungu adzathetsa bwanji mavutowa?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena