Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • yb14 tsamba 120
  • Baji Yawo Inali Ngati Pasipoti

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Baji Yawo Inali Ngati Pasipoti
  • Buku Lapachaka la Mboni za Yehova 2014
Buku Lapachaka la Mboni za Yehova 2014
yb14 tsamba 120

SIERRA LEONE AND GUINEA

Baji Yawo Inali Ngati Pasipoti

“MU 1987 anthu oposa 1,000 anafika pa msonkhano wachigawo wa mutu wakuti, ‘Khulupirirani Yehova’ womwe unachitikira ku Guékédou, m’dziko la Guinea. Popeza kuti malo a msonkhano anali m’malire a dziko la Sierra Leone ndiponso Liberia, anthu ena ankangoyendera kuchokera m’mayiko awiriwa. Komano vuto linali mapasipoti. Choncho abale ena anakambirana ndi akuluakulu a boma a m’malirewa ndipo anagwirizana zoti anthuwo azingosonyeza baji yawo n’kudutsa. Apolisi a m’malirewo akangoona baji yaolenji ankangoti dutsani.”—Everett Berry, yemwe anali mmishonale.

Abale ankalandira chakudya pa msonkhanowu

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena