Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • yb15 tsamba 42-tsamba 43 ndime 1
  • “Taona Zodabwitsa”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Taona Zodabwitsa”
  • Buku Lapachaka la Mboni za Yehova la 2015
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Kapolo Wokhulupirika Ndi Wanzeru Ndani?
    Kodi Ndani Akuchita Chifuniro cha Yehova Masiku Ano?
  • “Kapolo” Amene Ali Wokhulupirika ndi Wanzeru
    Nsanja ya Olonda—2004
  • “Ndani Kwenikweni Amene Ali Kapolo Wokhulupirika ndi Wanzeru?”
    Nsanja ya Olonda—2013
  • “Amatsatira Mwanawankhosa” Nthawi Zonse
    Nsanja ya Olonda—2009
Onani Zambiri
Buku Lapachaka la Mboni za Yehova la 2015
yb15 tsamba 42-tsamba 43 ndime 1
Zithunzi patsamba page 42

ZIMENE ZACHITIKA M’CHAKA CHAPITACHI

“Taona Zodabwitsa”

Zithunzi patsamba 43

Munthu wosaona akubatizidwa

TSIKU lina Yesu atachiritsa munthu wolumala, ‘anthu onse anadabwa kwambiri, ndipo anayamba kutamanda Mulungu, mwakuti anagwidwa ndi mantha. Iwo anali kunena kuti: “Taona zodabwitsa lero!”’ (Luka 5:25, 26) Masiku ano Yehova akuchita zambiri kudzera mwa Mwana wake, kapolo wokhulupirika ndi wanzeru komanso atumiki ake padziko lonse. Tikaganizira zonsezi timanenanso kuti: “Taona zodabwitsa.”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena