LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 14
  • Zinthu Zonse Zidzakhala Zatsopano

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zinthu Zonse Zidzakhala Zatsopano
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • ‘Apanga Zinthu Zonse Kukhala Zatsopano’
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tinadzipeleka kwa Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Yehova Ndiye Mfumu Yathu!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Yehova ndi Mfumu Yathu
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 14

Nyimbo 14

Zinthu Zonse Zidzakhala Zatsopano

(Chivumbulutso 21:1-5)

1. “Zizindikiro” zikusonyezadi

Kuti Yesu akulamulira.

Wapambana nkhondo ya kumwamba,

Posachedwa ayeretsa dziko.

(KOLASI)

Kondwa! Chifukwa Mulungu,

Alitu ndi anthu ake.

Sipadzakhalanso kulira,

Pena zopweteka ndi imfa;

Zidzakhala: ‘Zatsopano zonse.’

Mawuwa ndi oona.

2. Anthu aone Yerusalemuyo,

Mkwatibwi wa Mwanawankhosayo.

Atavala mochititsa chidwi,

Yehova ndiye kuwala kwake.

(KOLASI)

Kondwa! Chifukwa Mulungu,

Alitu ndi anthu ake.

Sipadzakhalanso kulira,

Pena zopweteka ndi imfa;

Zidzakhala: ‘Zatsopano zonse.’

Mawuwa ndi oona.

3. Mzindawu udzasangalatsa anthu.

Zipata zake sadzazitseka.

Anthu adzayenda muku’nika;

Atumikinu unikirani.

(KOLASI)

Kondwa! Chifukwa Mulungu,

Alitu ndi anthu ake.

Sipadzakhalanso kulira,

Pena zopweteka ndi imfa;

Zidzakhala: ‘Zatsopano zonse.’

Mawuwa ndi oona.

(Onaninso Mat. 16:3; Chiv. 12:7-9; 21:23-25.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani