LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 7
  • Tidzipereke Monga Akhristu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tidzipereke Monga Akhristu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tidzipeleka Monga Akhristu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • N’cifukwa Ciyani Muyenela Kudzipatulila kwa Yeehova?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2010
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 7

Nyimbo 7

Tidzipereke Monga Akhristu

(Aheberi 10:7, 9)

1. Yehova analengatu

Chilengedwe chonse,

Dzikoli ndi mlengalenga

Zonsezi ndi zake.

M’lungu watipatsa moyo

Wasonyeza kuti

Ndi woyenera kum’tamanda

Ndiponso kum’lambira.

2. Yesu anabatizidwa

Nanena m’pemphero:

‘Ndabwera kuti ndichite

Chifuniro chanu.’

Anatuluka m’Yo’dano

Monga wodzozedwa,

Kuti atumikire M’lungu

Monga wodzipereka.

3. Yehova, ife tabwera

Kukutamandani.

Tadzipereka kwa inu

Ndipo tadzikana.

Munapereka Mwana’nu,

Nalipira dipo.

Tasiyatu zofuna zathu,

Tizichitano zanu.

(Onaninso Mat. 16:24; Maliko 8:34; Luka 9:23.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani