LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 10
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Woyamba Kubadwa wa Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tamandani Mfumu Yatsopano Yodzalamulila Dziko
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • M’patseni Ulemelelo Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 10

NYIMBO 10

Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!

Yopulinta

(Salimo 145:12)

  1. 1. Imbani mosangalala!

    Lalikilani kwa onse:

    “Yehova, Atate wathu

    Adzalamulila kosatha!”

    Iye anasankha Yesu Khristu

    Kuti atilamulile.

    Uzani onse za madalitso

    Ufumu udzabweletsa.

    (KOLASI)

    Imbani mosangalala!

    Tamandani Yehova Mfumu!

  2. 2. Imbani, sekelelani!

    Lengezani za Yehova!

    Na mtima wosangalala

    Lalikilani za Ufumu.

    Yehova M’lungu ni wacifundo,

    Amasamalila onse.

    Ndipo iye ni wodzicepetsa,

    Amayankha mapemphelo.

    (KOLASI)

    Imbani mosangalala!

    Tamandani Yehova Mfumu!

(Onaninso Sal. 89:27; 105:1; Yer. 33:11.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani