LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 14
  • Tamandani Mfumu Yatsopano Yodzalamulila Dziko

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tamandani Mfumu Yatsopano Yodzalamulila Dziko
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tamandani Mfumu Yatsopano ya Dziko Lapansi
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tamandani Ya Kaamba ka Mwana Wake Wodzozedwayo
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 14

NYIMBO 14

Tamandani Mfumu Yatsopano Yodzalamulila Dziko

Yopulinta

(Salimo 2:12)

  1. 1. Anthu amitundu yonse asonkhana pamodzi,

    Waaitana ni Khristu na odzozedwa ake.

    Ufumu wa M’lungu wathu;

    Tsopano ulamulila.

    Tipempha cifunilo cake,

    Cicitike na padziko.

    (KOLASI)

    Tamandani Yehova; tamandani Yesu—

    Mfumu ya Mafumu onse.

    Capamodzi timuimbile iye

    Ni Mfumu yosatha.

  2. 2. Titamanda Khristu Mfumu yathu, mosangalala.

    Ni Kalonga wa Mtendele adzatipulumutsa.

    Taonani madalitso

    Ufumu udzabweletsa;

    Yesu adzautsa akufa.

    Tidzalumpha mokondwela!

    (KOLASI)

    Tamandani Yehova; tamandani Yesu—

    Mfumu ya Mafumu onse.

    Capamodzi timuimbile iye

    Ni Mfumu yosatha.

(Onaninso Sal. 2:6; 45:1; Yes. 9:6; Yoh. 6:40.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani