LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 9
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tamandani Woyamba Kubadwa wa Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tamandani Mfumu Yatsopano Yodzalamulila Dziko
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • M’patseni Ulemelelo Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 9

Nyimbo 9

Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!

(Salmo 145:12)

1. Tamanda! Yehova M’lungu!

Dzina lakelo lengeza!

Chenjeza! Adziwe kuti

Tsiku lake layandikira.

Mulungu walengeza za ulamuliro

Wa Mwana wake.

Kauzeni anthu uthengawu,

Ndi madalitso akenso!

(KOLASI)

Tamanda! Yehova M’lungu!

Lengeza kuti ndi wamkulu!

2. Tamanda! Mokweza mawu!

Mosangalala imbani!

Ndi mtima, woyamikira

Tilengeze ulemerero.

Mulungu ndi wamkulu kwambiri

Koma ndi wodzichepetsa,

Wokoma mtima ndi wachikondi,

Adzamva pemphero lathu.

(KOLASI)

Tamanda! Yehova M’lungu!

Lengeza kuti ndi wamkulu!

(Onaninso Sal. 89:27; 105:1; Yer. 33:11.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani