LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 47
  • Lalikirani Uthenga Wabwino

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Lalikirani Uthenga Wabwino
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Lengezani Uthenga Wabwino
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Cuma Capadela
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Cuma Capadela
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • “Uthenga Wabwino”!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 47

Nyimbo 47

Lalikirani Uthenga Wabwino

(Chivumbulutso 14:6, 7)

1. Poyamba sitinkadziwa za Ufumu.

Pano tikudziwa Mbewu yalonjezo.

Mwa chifundo ndi chikondi cha Yehova,

Anaganizira anthu ochimwafe.

Anakonza zoti Yesu alamule.

Ufumuwo unali woti udzabadwe.

Komanso kusankha kagulu ka nkhosa

Kadzakhale mkwatibwi wa Mwana wake.

2. Mulungu ankadziwa za uthengawu.

Tsopano afuna anthu audziwe.

Angelo amakondwa potithandiza

Kuchita ntchito yolengeza Ufumu.

Tilitu ndi udindo ndiponso mwayi

Wom’tamanda ndi kuyeretsa dzina lake.

Tili ndi mwayi wolengeza dzinalo

Mwa kulalikira uthenga wabwino.

(Onaninso Maliko 4:11; Mac. 5:31; 1 Akor. 2:1, 7.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani