LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • lfb masa. 218-219
  • Mawu Oyamba a Cigawo 14

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mawu Oyamba a Cigawo 14
  • Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Nkhani Zofanana
  • Masomphenya a Yohane
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Kodi Ufumu Wa Mulungu N’ciani?
    Zimene Baibulo Ingatiphunzitse
  • Kodi Ufumu wa Mulungu N’ciani?
    Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni-ceni
  • Coonadi Ponena za Ufumu wa Mulungu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2020
Onaninso Zina
Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
lfb masa. 218-219
Mtumwi Paulo na Timoteyo ali m’boti

Mawu Oyamba a Cigawo 14

Akhristu oyambilila analalikila uthenga wabwino wa Ufumu mpaka ku madela akutali kwambili pa dziko. Yesu anaŵauza kumene anafunika kukalalikila. Ndipo mozizwitsa anathandiza ophunzila ake kuphunzitsa anthu mu vitundu vawo. Yehova anawalimbitsa mtima kuti apilile pokumana na mazunzo oopsa.

Yesu anapatsa mtumwi Yohane masomphenya oona ulemelelo wa Yehova. M’masomphenya ena, Yohane anaona Ufumu wa kumwamba ukugonjetsa Satana na kuthetsa ulamulilo wake kwamuyaya. Yohane anaona Yesu akulamulila monga Mfumu pamodzi ndi anthu 144,000. Yohane anaona dziko lonse likusintha kukhala paradaiso, mmene aliyense anali kulambila Yehova mwamtendele, komanso mogwilizana.

MAPHUNZILO AKULU-AKULU M’CIGAWOCI

  • Kugwila nchito imene Yehova anatipatsa kumapeleka ulemelelo kwa iye

  • Patulilani moyo wanu kwa Yehova, ndipo muonetseni kuti mumafuna kukakhala mu Ufumu wake

  • Pangani Yehova kukhala Bwenzi lanu la pamtima

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani