LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w14 1/1 masa. 1-2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Tumitu
  • NKHANI ZOPHUNZILA
  • NKHANI ZOPHUNZILA
  • NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
w14 1/1 masa. 1-2

Zamkati

January 1, 2014

© 2014 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

NKHANI ZOPHUNZILA

MARCH 3-9, 2014

Lambilani Yehova, Mfumu Yamuyaya

TSAMBA 7 • NYIMBO: 106, 46

MARCH 10-16, 2014

Kodi Ulamulilo wa Yesu wa Zaka 100 Wakupindulitsani Bwanji?

TSAMBA 12 • NYIMBO: 97, 101

MARCH 17-23, 2014

Pangani Zosankha Mwanzelu Mukali Acinyamata

TSAMBA 17 • NYIMBO: 41, 89

MARCH 24-30, 2014

Tumikilani Yehova Asanafike Masiku Oipa

TSAMBA 22 • NYIMBO: 54, 17

MARCH 31, 2014–APRIL 6, 2014

“Ufumu Wanu Ubwele”—Kodi Udzabwela Liti?

TSAMBA 27 • NYIMBO: 108, 30

NKHANI ZOPHUNZILA

Lambilani Yehova, Mfumu Yamuyaya

Nkhani imeneyi idzatitsimikizila kuti Yehova nthawi zonse wakhala Mfumu ndipo idzaonetsa mmene wasonyezela ucifumu wake ku zolengedwa zake zakumwamba ndi za padziko lapansi. Nkhaniyi idzatilimbikitsanso kutsatila zitsanzo za anthu akale amene anasankha kulambila Yehova, Mfumu yamuyaya.

▪ Kodi Ulamulilo wa Yesu wa Zaka 100 Wakupindulitsani Bwanji?

Nkhaniyi idzatilimbikitsa kuyamikila kwambili zimene Ufumu wa Mesiya wakwanilitsa pa zaka 100 zoyambilila. Idzalimbikitsanso aliyense wa ife kukhalabe nzika yokhulupilika ya Ufumu, ndiponso idzatilimbikitsa kusinkha-sinkha tanthauzo la lemba la caka ca 2014.

▪ Pangani Zosankha Mwanzelu Mukali Acinyamata

▪ Tumikilani Yehova Asanafike Masiku Oipa

Kodi moyo wanga ndidzaugwilitsila nchito motani? Ili ndi funso lofunika kwambili limene wina aliyense amene anadzipeleka kwa Yehova ayenela kudzifunsa. M’nkhanizi, tidzakambilana mfundo zimene zingathandize Akristu acinyamata kutumikila Mulungu mokwanila ndiponso mipata imene Akristu acikulile ali nayo yoonjezela utumiki wao.

▪ Ufumu Wanu Ubwele”—Kodi Udzabwela Liti?

Anthu ambili masiku ano asokonezedwa ndi zimene zikucitika m’dzikoli kapena cifukwa cofuna-funa zinthu zakuthupi. Nkhaniyi idzafotokoza maumboni atatu amene amathandiza Akristu kukhulupilila kuti Ufumu wa Mulungu udzaononga dongosolo loipali posacedwapa.

NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO

Mphamvu ya Imfa 3

Zimene Anthu Acita Pofuna Kugonjetsa Imfa 4

Imfa Si Mapeto a Zonse 5

Kuyankha Mafunso a M’Baibo 32

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani