LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w14 7/15 masa. 1-2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Tumitu
  • YOPHUNZILA
  • NKHANI ZOPHUNZILA
  • NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
w14 7/15 masa. 1-2

Zamkati

July 15, 2014

© 2014 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

YOPHUNZILA

SEPTEMBER 1-7, 2014

“Yehova Amadziŵa Anthu Ake”

TSAMBA 7 • NYIMBO: 63, 66

SEPTEMBER 8-14, 2014

Anthu a Yehova “Aleke Kucita Zosalungama”

TSAMBA 12 • NYIMBO: 64, 61

SEPTEMBER 15-21, 2014

“Inu Ndinu Mboni Zanga”

TSAMBA 23 • NYIMBO: 31, 92

SEPTEMBER 22-28, 2014

“Mudzakhala Mboni Zanga”

TSAMBA 28 • NYIMBO: 102, 103

NKHANI ZOPHUNZILA

▪ “Yehova Amadziŵa Anthu Ake”

▪ Anthu a Yehova “Aleke Kucita Zosalungama”

Nkhani zimenezi zidzatithandiza kumvetsetsa lemba la 2 Timoteyo 2:19, ndipo zionetsa kuti lembali limagwilizana ndi zocitika za m’nthawi ya Mose. Tidzaphunzila mmene Akristu masiku ano, angaonetsele kuti ‘amadziŵika ndi Yehova,’ ndi kuti ‘aleka kucita zosalungama.’

▪ “Inu Ndinu Mboni Zanga”

▪ “Mudzakhala Mboni Zanga”

M’nkhanizi, tidzakambilana kufunika kokhala ndi dzina lakuti Mboni za Yehova. Tidzaphunzila kuti kunyadila nchito yocitila umboni za Yehova ndi Yesu kumafuna kuti tikhale acangu mu ulaliki. Kumafunanso kuti tizilemekeza Mulungu ndi Kristu ndi khalidwe lathu bwino.

NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO

3 Anadzipeleka Mofunitsitsa ku Micronesia

17 Kutaikilidwa Atate—Kupeza Atate

CIKUTO: Alongo aŵili agwilitsila nchito buku la Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni-ceni, polalikila kwa azimai aŵili acindebele amene avala zovala zacindebele. Iwo akhala patsogolo pa nyumba ya kamangidwe ka kumudzi wacindebele. Andebele ndi ocepa ku South Africa, ali cabe ciŵelengelo ca 2 pelesenti

SOUTH AFRICA

KULI ANTHU

50,500,000

OFALITSA ONSE

94,101

OFALITSA ACINDEBELE

1,003

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani