LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w15 7/15 masa. 1-2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Tumitu
  • YOPHUNZILA
  • NKHANI ZOPHUNZILA
  • NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
w15 7/15 masa. 1-2

Zamkati

July 15, 2015

© 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

YOPHUNZILA

AUGUST 31, 2015–SEPTEMBER 6, 2015

Thandizani Kukongoletsa Paladaiso Wauzimu

TSAMBA 7

SEPTEMBER 7-13, 2015

“Cipulumutso Canu Cikuyandikila”

TSAMBA 14

SEPTEMBER 14-20, 2015

Khalanibe Okhulupilika ku Ufumu wa Mulungu

TSAMBA 22

SEPTEMBER 21-27, 2015

Awa Ndi Malo Athu Olambilila

TSAMBA 27

NKHANI ZOPHUNZILA

▪ Thandizani Kukongoletsa Paladaiso Wauzimu

Anthu a Yehova akusangalala ndi paladaiso wauzimu amene ali m’mbali ya padziko lapansi ya gulu la Mulungu. Kodi tingasonyeze bwanji kuti timayamikila mphatso imeneyi yocokela kwa Yehova? Nanga aliyense wa ife angacite ciani kuti athandize kukongoletsa paladaiso ameneyu? Nkhaniyi iyankha mafunso amenewa.

▪ “Cipulumutso Canu Cikuyandikila”

Nkhaniyi ikufotokoza zinthu zabwino zimene tikuyembekezela posacedwapa. Ifotokozanso cifukwa cake tifunika kukhulupilila kuti Yehova adzatipulumutsa pa cisautso cacikulu.

▪ Khalanibe Okhulupilika ku Ufumu wa Mulungu

M’dziko la Satanali anthu ambili ndi okhulupilika ku dziko lao, fuko lao, ndi cikhalidwe cao. Koma, ife tinalonjeza Yehova kuti tidzakhala okhulupilika kwa iye. Nkhaniyi ifotokoza bwino cifukwa cake sititengamo mbali m’mikangano ya dzikoli ndiponso mmene tingaphunzitsile maganizo athu ndi cikumbumtima cathu kuti tisamatengemo mbali m’mikangano imeneyi.

▪ Awa Ndi Malo Athu Olambilila

Anthu a Yehova amakumana kuti alambile Mulungu mu Nyumba za Ufumu ndi malo ena masauzande ambilimbili padziko lonse lapansi. M’nkhaniyi tikambilana mfundo za m’Malemba zimene zidzatilimbikitsa kulemekeza malo amenewa ndi kupelekela ndalama zocilikizila nchito yomanga nyumbazi. Tikambilananso mmene tingasamalile malo amenewa kuti azipeleka ulemelelo kwa Yehova.

NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO

3 Anadzipeleka Mofunitsitsa—ku Russia

12 Kutumikila Yehova ‘m’Masiku Oipa’

20 Yehova Amaona Nchito Yanu

32 Kodi Mudziŵa?

PACIKUTO: Abale ndi alongo akudya cakudya ca masana pambuyo polalikila cigawo ca m’mawa ku madela a ku Siberia

KU RUSSIA

KULI ANTHU

143,930,000

OFALITSA

171,268

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani