LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w16 October tsa. 2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
w16 October tsa. 2

Zamkati

3 Mbili Yanga Kusiilana Citsanzo Cabwino

MLUNGU WA NOVEMBER 28, 2016–DECEMBER 4, 2016

8 “Musaiŵale Kuceleza Alendo”

MLUNGU WA DECEMBER 5-11, 2016

13 Khalanibe Auzimu Potumikila Mumpingo wa Cinenelo Cina

Masiku ano, m’mipingo yathu muli anthu a mitundu yosiyana-siyana ndiponso a kumaiko ena. Nkhani yoyamba idzatithandiza kudziŵa mmene tingaonetsele cikondi ceni-ceni kwa anthu a kumaiko ena amene amasonkhana nafe. Nkhani yaciŵili ifotokoza zimene anthu otumikila mumpingo wa cinenelo cina angacite kuti akhalebe auzimu.

18 Kodi ‘Mumasunga Nzelu Zopindulitsa’?

MLUNGU WA DECEMBER 12-18, 2016

21 Limbitsani Cikhulupililo Canu pa Zimene Muyembekezela

MLUNGU WA DECEMBER 19-25, 2016

26 Khalani na Cikhulupililo m’Malonjezo a Yehova

Nkhani zimenezi zifotokoza bwino mbali ziŵili za cikhulupililo zofotokozedwa pa Aheberi 11:1. Nkhani yoyamba ionetsa mmene cikhulupililo cingakulile na kukhalabe colimba. Nkhani yaciŵili ifotokoza cifukwa cake cikhulupililo si kumvetsetsa cabe madalitso amene Yehova adzatipatsa.

31 KODI MUDZIŴA?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani