LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w16 December tsa. 2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
w16 December tsa. 2

Zamkati

3 Mbili Yanga​—Kukhala “Zinthu Zonse Kwa Anthu Osiyana-siyana”

MLUNGU WA JANUARY 30, 2017–FEBRUARY 5, 2017

8 Tinamasulidwa mwa Cisomo ca Mulungu

MLUNGU WA FEBRUARY 6-12, 2017

13 ‘Kuika Maganizo Athu pa Zinthu za Mzimu Kumabweletsa Moyo na Mtendele’

M’caputa 6 na 8 ca Aroma, muli malangizo ofunika okhudza umoyo wa ise Akhiristu. Kuphunzila malemba amenewo kudzatithandiza kupindula na cisomo ca Mulungu ndi kuikabe maganizo athu pa zinthu zimene zidzatipindulitsa kwamuyaya.

18 KodI Mukumbukila?

MLUNGU WA FEBRUARY 13-19, 2017

19 Tulilani Yehova Nkhawa Zanu Zonse

MLUNGU WA FEBRUARY 20-26, 2017

24 Yehova Amapeleka Mphoto kwa Anthu Omufuna-funa na Mtima Wonse

Nkhani yoyamba idzafotokoza mmene tingatulile Mulungu nkhawa zathu. Nkhani yaciŵili idzafotokoza mmene tingalimbitsile cikhulupililo cathu mwa kukhala otsimikiza na mtima wonse kuti Mulungu amadalitsa anthu amene amam’funa-funa na mtima wonse. Idzaonetsanso mmene tingapindulile na ciyembekezo codzalandila mphoto.

29 Kufatsa—Kumaonetsa Nzelu

32 MLONGOZA NKHANI WA NSANJA YA MLONDA 2016

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani