LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 10/12 tsa. 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 8

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 8
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Tumitu
  • MLUNGU WA OCTOBER 8
Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
km 10/12 tsa. 1

Ndandanda ya Mlungu wa October 8

MLUNGU WA OCTOBER 8

Nyimbo 75 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 13 ndime 8-16, bokosi pa tsa. 105 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Danieli 7-9 (Mph. 10)

Na. 1: Danieli 7:13-22 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Baibo Imasonyeza Kuti Akristu Oona Adzalinganizidwa Kukhala Gulu?—rs tsa. 141 ndime 2-tsa. 142 ndime 2 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Yehova ndi Wokhulupilika M’njila Zanji?—Chiv. 15:4; 16:5 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 133

Mph. 10: Ngati munthu akamba kuti, ‘Ndine Wotangwanika’ Kukambilana kozikidwa pa buku la Kukambitsirana, tsamba 19, ndime 5, mpaka tsamba 20 ndime 4. Kambilanani mayankhidwe ena amene apelekedwa m’bukuli ndi ena omwe agwilitsidwapo nchito mogwila mtima m’gawo lanu. Khalani ndi zitsanzo ziŵili zacidule.

Mph. 10: Tiphunzilapo Ciani? Kukambilana. Malemba awa aŵelengedwe: Mateyu 21:12-16 ndi Luka 21:1-4. Kambilanani zimene tiphunzilapo pa Malembawa.

Mph. 10: “Kodi Mukhoza Kumacitako Ulaliki wa M’madzulo?” Mafunso ndi mayankho. Pokambilana ndime 2, pemphani omvela kuti asimbe zocitika zimene anasangalala nazo muulaliki wa m’madzulo.

Nyimbo 92 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani