LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 10/12 tsa. 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 15

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 15
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Tumitu
  • MLUNGU WA OCTOBER 15
Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
km 10/12 tsa. 2

Ndandanda ya Mlungu wa October 15

MLUNGU WA OCTOBER 15

Nyimbo 101 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 13 ndime 17-24 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Danieli 10-12 (Mph. 10)

Na. 1: Danieli 11:15-27 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Cifukwa Cake Akristu Sabwezela Coipa—Aroma 12:18-21 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Atumiki a Mulungu Okhulupilika Amapezeka M’machalichi Osiyana-siyana Acikristu?—rs tsa. 142 ndime 3-5 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 106

Mph. 10: Ngati munthu anena kuti, ‘Sindifuna.’ Kukambilana kozikidwa pa buku la Kukambitsilana, tsamba 16, ndime 1, mpaka tsamba 18, ndime 1. Kambilanani mayankhidwe ena amene alembedwa m’bukumo, ndiponso ena amene agwilitsilidwapo nchito mogwila mtima m’gawo la kwanuko. Citani zitsanzo ziŵili zoonetsa mmene tingayankhile.

Mph. 20: “Gwilitsilani Nchito Tumapepala twa Uthenga Kufalitsa Uthenga Wabwino.” Mafunso ndi Mayankho. Pokambilana ndime 5, fotokozani mwacidule tumapepala twa uthenga togaŵila m’mwezi wa November, ndipo citani citsanzo cogaŵila kapepala kamodzi. Pokambilana ndime 7, khalani ndi citsanzo cogwilitsila nchito tumapepala twa uthenga muulaliki wamwai.

Nyimbo 97 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani