LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 11/12 tsa. 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 19

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 19
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Tumitu
  • MLUNGU WA NOVEMBER 19
Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
km 11/12 tsa. 2

Ndandanda ya Mlungu wa November 19

MLUNGU WA NOVEMBER 19

Nyimbo 81 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 15 ndime 8-12, ndi bokosi patsamba 118 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Obadiya 1–Yona 4 (Mph. 10)

Na. 1: Yona 2:1-10 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Kulambila Koona Kumathandiza Bwanji Kuti Anthu Amitundu Yonse Akhale Ogwilizana?—Sal. 133:1 (Mph. 5)

Na. 3: N’cifukwa Ciani “Paladaiso” Wochulidwa pa Luka 23:43 Sangakhale Mbali Ina ya Hade Kapena ya Kumwamba?—rs tsa. 337 ndime 1-tsa. 338 ndime 1 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 95

Mph. 15: Kutumikila ku Malo Osoŵa Kumabweletsa Madalitso a Yehova. Kukambilana kozikidwa pa Nsanja ya Olonda ya October 15, 2012, masamba 3 mpaka 6. Pemphani omvela kuti akambepo zimene aphunzilapo.

Mph. 15: “Mungakwanitse—Musadzidelele.” Mafunso ndi mayankho. Funsani mwacidule munthu amene sanaphunzile kwambili, kapena wamanyazi koma amatsogoza maphunzilo a Baibo.

Nyimbo 26 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani