LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 11/12 tsa. 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 26

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 26
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Tumitu
  • MLUNGU WA NOVEMBER 26
Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
km 11/12 tsa. 3

Ndandanda ya Mlungu wa November 26

MLUNGU WA NOVEMBER 26

Nyimbo 62 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 15, bokosi patsamba 121 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Mika 1-7 (Mph. 10)

Na. 1: Mika 3:1-12 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi N’ciani Cikusonyeza Kuti Paladaiso Wochulidwa pa Luka 23:43 Adzakhala Padziko Lapansi Pompano?—rs tsa. 338 ndime 2-tsa. 339 ndime 2 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Timadziŵa Bwanji Kuti Yehova Ndi Wakumva Pemphelo?—1Yoh. 5:14 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 56

Mph. 5: Yambitsani Phunzilo la Baibo pa Ciŵelu Coyamba. Mwa kugwilitsila nchito ulaliki wacitsanzo uli patsamba 4, onetsani mmene tingayambitsile phunzilo pa Ciŵelu coyamba mu December. Limbikitsani onse kutengako mbali.

Mph. 10: Zoculuka Zao Zinathandizila Osowa. Nkhani yokambidwa ndi mkulu yozikidwa pa Nsanja ya Olonda ya November 15, 2012 masamba 8-9.

Mph. 15: “Mungakwanitse—Ngakhale Muli ndi Zocita Zambili.” Mafunso ndi mayankho. Kambilananinso mwacidule ndi wofalitsa amene amatsogoza maphunzilo ngakhale kuti ali ndi zocita zambili.

Nyimbo 73 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani