LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 12/12 tsa. 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa December 17

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa December 17
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Tumitu
  • MLUNGU WA DECEMBER 17
Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
km 12/12 tsa. 2

Ndandanda ya Mlungu wa December 17

MLUNGU WA DECEMBER 17

Nyimbo 97 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 16 ndime 8-12, ndi bokosi patsamba 132 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Zekariya 1-8 (Mph. 10)

Na. 1: Zekariya 8:1-13 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Tingasonyeze Bwanji Kuti Yehova Ndi Ambuye Wamkulu Koposa?—Sal. 73:28 (Mph. 5)

Na. 3: N’cifukwa Ciani Anthu Oganiza Bwino Amaphunzila Zimene Yesu Kristu Ankaphunzitsa, M’malo Mwa Nzelu za Anthu?—rs tsa. 138 ndime 1–tsa. 139 ndime 1 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 65

Mph. 5: “Zimene Mungakambe Pogaŵila Magazini mu . . .” Kukambilana.

Mph. 10: Uthenga Umene Tiyenela Kulengeza—‘Opani Mulungu Woona, Sungani Malamulo Ake.’ Nkhani yogwila mtima yocokela m’buku la Sukulu ya Utumiki, patsamba 272, mpaka pa kamutu patsamba 275.

Mph. 15: Kodi Mwayesapo Kuzigwilitsila Nchito? Kukambilana. Kambani nkhani yacidule yofotokoza mfundo zazikulu za nkhani izi za mu Utumiki Wathu wa Ufumu waposacedwa: “Muzilalikila Molimba Mtima Kumalo a Nchito ndi Amalonda” (km 3/12) “Thandizani Anthu Kuti Azimvela Mulungu” (km 8/12), ndi “Kodi Mukhoza Kumacitako Ulaliki wa M’madzulo?” (km 10/12). Kenako pemphani omvela kuti akambe mapindu amene apeza mwa kugwilitsila nchito malingalilo a mu nkhani zimenezi.

Nyimbo 117 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani