LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 12/12 tsa. 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa December 24

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa December 24
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Tumitu
  • MLUNGU WA DECEMBER 24
Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
km 12/12 tsa. 2

Ndandanda ya Mlungu wa December 24

MLUNGU WA DECEMBER 24

Nyimbo 5 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 16 ndime 13-18 (Mph.30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Zekariya 9–14 (Mph.10)

Na. 1: Zekariya 11:1-13 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Mulungu Amakhala Wofunitsitsa Kumva Mapemphelo a Anthu Otani?—rs tsa. 339 ndime 3-tsa. 340 ndime 6 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Tingagwilitse Nchito Mfundo ya pa Miyambo 15:1 pa Nthawi Iti? (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 75

Mph. 10: Tiyeni Tigwilitsile Nchito Bwino Webu Saiti Yathu. Nkhani yocokela mu mphatika pa masamba 3-6. Dziŵitsani abale za Webu Saiti yathu ya jw.org. Ngati abale sadziŵa za makompyuta, limbikitsani mabanja kukhala ndi laibulale yaing’ono ya mabuku athu kunyumba kwao. Muwalimbikitse kucita zimenezi mukatsiliza kufotokoza mwacidule mfundo za m’mphatika.

Mph. 10: Mabanja Acikristu, Khalani Maso. Nkhani ndi mbali yofunsa mafunso, yozikidwa pa Nsanja ya Olonda ya May 15, 2011, masamba 7 mpaka 11. Pambuyo pofotokoza mwacidule nkhaniyo kwa mphindi 5, kambilanani ndi tate, mai ndi wacinyamata. Apempheni kufotokoza zimene amacita kuti alimbitse uzimu wa banja lao.

Mph. 10: Kodi Mukupindula ndi Kulambila kwa Pabanja? Nkhani ndi kukambilana ndi omvela, yozikidwa pa Nsanja ya Olonda ya August 15, 2011 tsamba 6. Funsani omvela kuti afotokoze njila zimene aona kuti n’zothandiza pa kulambila kwao kwa pabanja ndi cifukwa cake njilazo n’zothandiza.

Nyimbo 101 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani