LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 12/12 tsa. 7
  • Ndandanda ya Mlungu wa December 31

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa December 31
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Tumitu
  • MLUNGU WA DECEMBER 31
Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
km 12/12 tsa. 7

Ndandanda ya Mlungu wa December 31

MLUNGU WA DECEMBER 31

Nyimbo 60 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 17 ndime 1-7 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Malaki 1-4 (Mph. 10)

Kubweleza za m’Sukulu ya Ulaliki (Mph. 20)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 72

Mph. 10: “Nkhani Yatsopano Imene Izipezeka mu Nsanja ya Olonda.” Nkhani. Gwilitsilani nchito ulaliki wacitsanzo umene uli patsamba 8, kuti muonetse mmene mungagwilitsilile nchito magazini poyambitsa phunzilo la Baibo pa Ciŵelu coyamba mu January.

Mph. 10: Kodi Tiphunzilapo Ciani? Kukambilana. Lemba la Luka 10:38-42 liŵelengedwe. Kambilanani mmene nkhani ili pa lembali ingatithandizile mu ulaliki.

Mph. 10: Cogaŵila ca mu January ndi February. Kukambilana. Kambilanani mfundo zina mu cofalitsa cimene tigaŵila, ndipo khalani ndi zitsanzo ziŵili.

Nyimbo 134 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani