LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 1/13 tsa. 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa January 14

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa January 14
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Tumitu
  • MLUNGU WA JANUARY 14
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 1/13 tsa. 1

Ndandanda ya Mlungu wa January 14

MLUNGU WA JANUARY 14

Nyimbo 52 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 17 ndime 15-19 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Mateyu 7-11 (Mph. 10)

Na. 1: Mateyu 10:24-42 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Muzicita Zinthu Mwanzelu Ndipo Muzipewa Zinthu Zopanda Pake—1 Sam. 12:21; Miy. 23:4, 5 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi ndi Zinthu Ziti Zimene Tiyenela Kuchula Tikamapemphela?—rs tsa. 341 ndime 8–tsa. 342 ndime 6 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 73

Mph. 10: Athandizeni pa Zosoŵa Zao. Nkhani yocokela m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 188, ndime 4, mpaka tsamba 189, ndime 4. Mwacidule funsani wofalitsa amene wapita patsogolo cifukwa cakuti ena anamuonetsa cidwi.

Mph. 10: Kodi Tiphunzilapo Ciani? Kukambilana. Lemba la Mateyu 4:1-11 liŵelengedwe. Kambilanani mmene nkhani ili pa lembali ingatithandizile mu ulaliki.

Mph. 10: “Citilani Umboni Mokwanila.” Mafunso ndi mayankho.

Nyimbo 92 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani