LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 3/13 tsa. 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa March 11

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa March 11
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Tumitu
  • MLUNGU WA MARCH 11
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 3/13 tsa. 1

Ndandanda ya Mlungu wa March 11

MLUNGU WA MARCH 11

Nyimbo 68 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 20 ndime 1-7, onani bokosi pa tsa. 156 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Maliko 13–16 (Mph. 10)

Na. 1: Maliko 14:22-42 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: N’cifukwa Ciani Tiyenela Kukumbukila Imfa ya Yesu?—rs tsa. 70 ndime 3-tsa. 71 ndime 2 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Zizindikilo za pa Cikumbutso Zimaimila Ciani?—rs tsa. 71 ndime 2-tsa. 72 ndime 2 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 109

Mph. 10: Tiphunzilapo Ciani? Ŵelengani Mateyu 10:7-10 ndi Luka 10:1-4, ndipo kambilanani mmene malembawa angatithandizile mu utumiki.

Mph. 10: Njila Zoonjezela Utumiki Wanu—Gawo 1. Nkhani yokambilana yocokela m’buku la Gulu, patsamba 111, ndime 1, mpaka tsamba 112, ndime 2. Funsani wofalitsa mmodzi kapena aŵili amene asamukila ku dela lina kapena amene aphunzila cinenelo cina n’colinga coonjezela utumiki wao. Kodi anakumana ndi mavuto otani? Ndipo anacita bwanji kuti awathetse? Kodi banja lao kapena mpingo unawathandiza bwanji? Kodi apeza madalitso otani?

Mph. 10: “Konzekelani Cikumbutso ndi Mtima Wacimwemwe.” Nkhani ya mafunso ndi mayankho. Chulani makonzedwe a Cikumbutso amene mpingo wapanga. Pelekani lipoti loonetsa mmene nchito yoitanila anthu ku Cikumbutso ikuyendela pampingo panu.

Nyimbo 8 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani