LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 10/13 tsa. 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 14

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 14
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Tumitu
  • MLUNGU WA OCTOBER 14
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 10/13 tsa. 1

Ndandanda ya Mlungu wa October 14

MLUNGU WA OCTOBER 14

Nyimbo 32 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

jl phunzilo 11 mpaka 13 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Afilipi 1 mpaka Akolose 4 (Mph. 10)

Na. 1: Afilipi 3:17 mpaka 4:1-9 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi N’zoyenela Kusiya Cipembedzo Cimene Munabadwila?—rs tsa. 85 ndime 2 mpaka 4 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Pemphelo Lingatithandize Bwanji Kuthana Ndi Mayeselo?—Luka 11:9-13; Yak. 1:5 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 68

Mph. 15: Umodzi Wathu Wapadziko Lonse Umalemekeza Yehova. Nkhani yocokela m’buku la Gulu, tsamba 165, ndime 2, mpaka tsamba 168. Pemphani ena m’gulu kuti afotokoze zocitika mu utumiki zimene anaŵelenga m’zofalitsa zathu zimene zimaonetsa mmene umodzi ndi cikondi ca Mboni za Yehova cinathandizila kucitila umboni.

Mph. 15: “Tidzagaŵila kapepala ka Uthenga wa Ufumu Na. 38 mu November.” Mafunso ndi Mayankho. Gaŵilani aliyense m’gulu kapepala kamodzi ka Uthenga wa Ufumu Na. 38. Pemphani woyang’anila nchito kuti afotokoze makonzedwe amene alipo ogaŵila kapepala ka uthenga m’gawo lanu. Mwa kugwilitsila nchito ulaliki wacitsanzo uli patsamba 4, onetsani mmene tingagaŵile kapepala ka Uthenga wa Ufumu.

Nyimbo 53 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani