LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 10/13 tsa. 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 4

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 4
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Tumitu
  • MLUNGU WA NOVEMBER 4
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 10/13 tsa. 4

Ndandanda ya Mlungu wa November 4

MLUNGU WA NOVEMBER 4

Nyimbo 116 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

jl phunzilo 20 mpaka 22 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Tito 1 mpaka Filimoni (Mph. 10)

Na. 1: Tito 2:1-15 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Mumaona Kuti N’zoyenela Kukhala M’cipembedzo Cinacake?—rs tsa. 87 ndime 2 mpaka tsa. 88 ndime 1 (Mph. 5)

Na. 3: N’cifukwa Ciani Sitiyenela ‘Kumvetsela Nkhani Zonama’?—1 Tim. 1:3, 4; 2 Tim. 4:3, 4 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 95

Mph. 10: Zimene Mungakambe Pogaŵila Magazini mu November. Kukambilana mogwilitsila nchito mafunso otsatilawa: Ngati n’kotheka, cifukwa ciani tiyenela kugaŵilanso magazini pamene tigaŵila tumapepala twa Uthenga wa Ufumu Na. 38 kumapeto kwa mlungu? Ndi liti pamene tingacite zimenezi? Kodi tingakambe ciani pogaŵila magazini pambuyo pakuti tagaŵila kapepala ka Uthenga wa Ufumu? Citani citsanzo coonetsa mmene magazini iliyonse ingagaŵilidwe pamodzi ndi kapepala ka Uthenga wa Ufumu Na. 38.

Mph. 10: Zosoŵa za pampingo.

Mph. 10: Mau a Mulungu ndi Amphamvu. (Aheb. 4:12) Kukambilana kocokela mu buku lapacaka la Mboni za Yehova la 2013, tsamba 57 ndime 1, mpaka tsamba 59, ndime 3. Pemphani omvela kuti afotokoze zimene aphunzilapo.

Nyimbo 114 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani