LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 11/13 tsa. 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 11

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 11
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Tumitu
  • MLUNGU WA NOVEMBER 11
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 11/13 tsa. 1

Ndandanda ya Mlungu wa November 11

MLUNGU WA NOVEMBER 11

Nyimbo 119 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

jl Phunzilo 23 mpaka 25 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Aheberi 1 mpaka 8 (Mph. 10)

Na. 1: Aheberi 4:1-16 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Tingasonyeze Bwanji Kuti Tili Ndi “Nzelu Yocokela Kumwamba”?—Yak. 3:17, 18 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Cofunikila Kwa Akristu Ndi Kukonda Anzawo Basi?—rs tsa. 88 ndime 3 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 73

Mph. 10: Mmene Tingathandizile Kusamalila Zosoŵa za Ena. Nkhani yokambidwa ndi mkulu yocokela mu Nsanja ya Olonda ya November 15, 2013, tsamba 8 ndi 9.

Mph. 10: Mmene Tingathetsele Mantha Polalikila. Kukambitsilana kozikidwa pa mafunso otsatilawa: (1) Kodi pemphelo lingatithandize bwanji tikacita mantha pamene tilalikila pakhomo? (2) N’cifukwa ciani kukonzekela bwino kumatithandiza kucepetsa mantha? (3) N’ciani cingatithandize kucepetsa mantha pamene tilalikila ndi woyang’anila dela? (4) Kodi kulalikila mokhazikika kumatithandiza bwanji kucepetsa mantha? (5) N’ciani cakuthandizani kuthetsa mantha?

Mph. 10: “Tengelani Citsanzo kwa Aneneli—Hoseya.” Mafunso ndi mayankho.

Nyimbo 113 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani