LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 2/14 tsa. 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa February 24

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa February 24
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tumitu
  • MLUNGU WA FEBRUARY 24
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 2/14 tsa. 3

Ndandanda ya Mlungu wa February 24

MLUNGU WA FEBRUARY 24

Nyimbo 101 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 5 ndime 1 mpaka 6, ndi bokosi patsamba 55 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: Genesis 32-35 (Mph. 10)

Kubweleza za m’Sukulu ya Ulaliki (Mph. 20)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 96

Mph. 5: Kuyambitsa Phunzilo la Baibulo pa Ciŵelu Coyamba. Nkhani. Chulani makonzedwe a ulaliki amene mpingo wapanga pa Ciŵelu coyamba mu March. Citani citsanzo cimene cili patsamba 4.

Mph. 15: Cifukwa Cake Kulimbikila N’kofunika. Nkhani yokambitsilana yocokela mu Buku Lapacaka la 2013 tsamba 45, ndime 1, mpaka tsamba 46, ndime 1; ndi masamba 136 mpaka 137. Pemphani omvela kuti afotokoze zimene aphunzilapo.

Mph. 10: “Tidzayamba Kuitanila Anthu ku Cikumbutso pa March 22.” Nkhani yokambidwa ndi woyang’anila nchito. Gaŵilani tumapepala toitanila anthu ku Cikumbutso ndi kukambitsilana mfundo zake. Bwelelani m’malangizo othandiza a m’kalata ya akulu, ndi kuchula makonzedwe a mpingo ofola gawo lonse.

Nyimbo 109 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani