LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 3/14 tsa. 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa March 24

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa March 24
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tumitu
  • MLUNGU WA MARCH 24
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 3/14 tsa. 3

Ndandanda ya Mlungu wa March 24

MLUNGU WA MARCH 24

Nyimbo 104 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 6 ndime ¶7-12, ndi bokosi patsamba 73 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: Genesis 47-50 (Mph. 10)

Na. 1: Genesis 48:17 mpaka 49:7 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Zocitika Zosonyeza Kukhalapo kwa Kristu Zimatenga Nyengo ya Zaka Zambili—rs tsa. 162 ndime 1-2 (Mph. 5)

Na. 3: Kudzikuza Kumabweletsa Mavuto (Miy. 11:2; 1 Pet. 5:5-7) (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 56

Mph. 10: Tsatilani Citsanzo ca Nehemiya. Kukambitsilana. Pemphani omvela kuti afotokoze zimene akuphunzila pa citsanzo ca Nehemiya monga alaliki.

Mph. 10: Gwilitsilani Nchito Mafunso Kuti Muphunzitse Mogwila Mtima—Mbali 1. Nkhani yokambitsilana yocokela m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 236, mpaka tsamba 237, ndime 2. Citani citsanzo cacidule cosonyeza mfundo imodzi ya m’nkhani.

Mph. 10: Yehova Amamvetsela Mapemphelo a Olungama. (1 Pet. 3:12) Nkhani yokambitsilana yocokela mu Buku Lapacaka la 2013, tsamba 66, ndime 1-3; ndi masamba 104 mpaka 105. Pemphani omvela kuti afotokoze zimene aphunzilapo.

Nyimbo 6 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani