LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 3/14 tsa. 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa April 7

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa April 7
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tumitu
  • MLUNGU WA APRIL 7
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 3/14 tsa. 4

Ndandanda ya Mlungu wa April 7

MLUNGU WA APRIL 7

Nyimbo 15 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 6 ¶19-24, ndi bokosi patsamba 78 (30 min.)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: Ekisodo 7–10 (Mph. 10)

Na. 1: Ekisodo 9:20 mpaka 35 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Mmene Kubwela kwa Yesu Kudzakhalile Ndiponso Mmene Diso Lililonse Lidzamuonele—rs tsa 163 ndime 3 mpaka tsa. 164 ndime 4 (Mph. 5)

Na. 3: Muzikhala Wokhulupilika Ndiponso Wokonzeka Kuthandiza Abale Anu—lv tsa. 33 mpaka 34 ndime 16-18. (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 124

Mph. 10: Kugaŵila Magazini m’Mwezi wa April. Nkhani yokambitsilana. Yambani nkhaniyi mwa kucita citsanzo ca zimene tingacite pogaŵila magazini. Gwilitsilani nchito maulaliki acitsanzo amene ali patsamba lino. Ndiyeno kambitsilanani maulaliki onse acitsanzo. Mwacidule malizani mwa kulimbikitsa onse kuti aziŵelenga magazini ndi kuwagaŵila kwa ena mokondwela.

Mph. 10: Musaiŵale Kuceleza Alendo. (Aheb. 13:1, 2) Nkhani yokambidwa ndi mkulu. Fotokozani makonzedwe amene mpingo wapanga kaamba ka Cikumbutso. Chulani zimene onse angacite kuti akaceleze alendo ndi ofalitsa ozilala amene adzapezeka pa Cikumbutso. Citani citsanzo cacidule ca mbali ziŵili. Citsanzo coyamba, cionetse wofalitsa akulandila munthu amene analandila ciitano cobwela ku Cikumbutso, wofalitsa akucita zimenezi misonkhano isanayambe. Caciŵili, pambuyo pa misonkhano wofalitsa akupanga makonzedwe okacezela mlendo amene anaonetsa cidwi.

Mph. 10: Kodi Tinacita Zotani? Nkhani yokambitsilana. Pemphani omvela kuti afotokoze mapindu amene apeza pogwilitsila nchito mfundo za m’nkhani yakuti, “Kuongolela Luso Lathu mu Ulaliki—Mmene Tingayankhile Anthu Amene Safuna Kuti Tikambitsilane Nao.” Pemphani omvela kuti asimbe zocitika zabwino za mu ulaliki.

Nyimbo 20 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani