LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 9/14 tsa. 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa September 8

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa September 8
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tumitu
  • MLUNGU WA SEPTEMBER 8
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 9/14 tsa. 1

Ndandanda ya Mlungu wa September 8

MLUNGU WA SEPTEMBER 8

Nyimbo 133 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 13 ndime 8 mpaka 13 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: Numeri 22-25 (Mph. 10)

Na. 1: Numeri 22:36 mpaka 23:1-10 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Satana Si Maganizo Oipa Cabe Amene Anthu Angakhale Nao—rs tsa. 353 ndime 2-4 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Adamu Analengedwa m’Cifanizilo ca Mulungu m’Njila Iti?—(Gen 1:26) (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 94

Mph. 15: Sonyezani Khalidwe Labwino mu Ulaliki. (2 Akor. 6:3) Gwilitsani nchito mafunso otsatilawa pokambilana: (1) N’cifukwa ciani tiyenela kusonyeza makhalidwe abwino tikamalalikila? (2) Tingasonyeze bwanji makhalidwe abwino (a) gulu lathu likafika m’gawo limene timalalikila? (b) tikamayenda nyumba ndi nyumba? (c) tikaima pakhomo la mwininyumba? (d) mnzathu akamalalikila? (e) mwininyumba akamalankhula? (f) tikapeza mwininyumba wotangwanika kapena ngati nyengo sili bwino? (g) ngati mwininyumba ndi wamwano?

Mph. 15: “Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Kuyala Maziko a Ulendo Wobwelelelako.” Nkhani yokambilana. Mukhalenso ndi citsanzo coonetsa wofalitsa akukamba yekha pokonzekela utumiki wakumunda. Pokonzekelapo, iye akukonza funso lakuti akafunse mwininyumba akadzavomela kutenga magazini.

Nyimbo 68 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani